KULENGEZA ZOTSATIRA ZA KAWUNIWUNI WA MOMWE NTCHITO YOMANGA MA SIKIMU A LINGONI KOMANSO NKHULAMBE/WOWO  ZINGAKHUDZIRE CHILENGEDWE KOMANSO UMOYO WA ANTHU

0 Comments

  • Version
  • Download 0
  • File Size 131.97 KB
  • File Count 1
  • Create Date April 11, 2021
  • Last Updated April 11, 2021

KULENGEZA ZOTSATIRA ZA KAWUNIWUNI WA MOMWE NTCHITO YOMANGA MA SIKIMU A LINGONI KOMANSO NKHULAMBE/WOWO  ZINGAKHUDZIRE CHILENGEDWE KOMANSO UMOYO WA ANTHU

KULENGEZA ZOTSATIRA ZA KAWUNIWUNI WA MOMWE NTCHITO YOMANGA MA SIKIMU A LINGONI KOMANSO NKHULAMBE/WOWO  ZINGAKHUDZIRE CHILENGEDWE KOMANSO UMOYO WA ANTHU

Boma la Malawi kudzera ku Unduna waza Ulimi lalandira ngongole komanso thandizo la ndalama kuchokera ku Bungwe la International Fund for Agriculture Development (IFAD) zomangira ma sikimu kudzera ku Pulojekiti ya PRIDE. Boma la Malawi lalandiranso thandizo la ndalama kuchokera ku Bungwe la Global Environmental Facility (GEF) zogwilira ntchito yolimbikitsa ntchito za ulimi yotchedwa ERASP. Unduna waza Ulimi kudzera ku Nthambi ya Ulimi Wanthilira ukufuna kugwiritsa ntchito mbali ina ya ndalamazi kukonza ma pulani komanso kumanga ma Sikimu a Lingoni m’boma la Machinga komanso Nkhulambe/Wowo m’boma la Phalombe.

Categories:

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *